Pastor Demba follows
Preaching word of God
Wina aliyese amene anatembelera dzina lako kuti uzikhala ndi moyo odwaladwala muchaka chino ndikulamula mudzina lambuye wanthu yesu kristu kuti back to sender.
Landila chisomo mudzina lambuye wanthu yesu kristu Amen.
Ndikunenela moyo wako kuti usiku uno matenda omwe ukudwala mulungu akukhudze ndikulandila machilitso mudzina lambuye wanthu yesu kristu Amen
Ndikulamula matsoka,minyama, matsenga, matemberero, umphawi, ngozi,ifa zomwe anaziika padzina lako ndikusamutsa mudzina lambuye wanthu yesu kristu kuti zisatenge gawo ndi ulamuliro mwa iwe.
Ukamakhala udziwe kuti sionse omwe amakufunila zabwino pamoyo wako.koma mulungu amapanga njira yokupambanitsa kuti oipayo achite manyazi (usaope ompha thupi koma opa ompha mzimu)
USIKU walero mulungu akumane ndimoyo wako ndikusitha komaso kuchotsa chitozo pamoyo wako.mudzina la mbuye wanthu yesu kristu
Ndingofuna tikumbutsane kuti ulendo wopita kumwamba sitidzatenga China chilichose monga tichitila ulendo wakudziko ayi,paulendo wakumwamba aliyense adzayenda ndi m'tima basi,Kodi ndichifukwa chiyani anthu Ife timalimbana ndi katundu wadziko?
YAKHO
Chifukwa chakuti tilibe maso akuzimu omwe angationetse pa chabwino komaso choipa.
PHUZIRO
Tiyeni titaye zonse zakudziko lapansi kuti paulendo opita kumwamba tisadzakhale otanganidwa AMBUYE AKHALE NANU POMWE MUKUZIYESA NTCHITO ZAKUDZIKO LAPANSI KUTI ZOPANDA PHINDU AMEN.
Ndaona iweyo ukulila chifukwa choti wina sanakwanilitse malonjezano ake pamoyo wako, ndifuna ndikulimbitse m'tima kuti usalire ndizomwe muthu nzako analonjeza pa iwe. dziwa kuti munthu ndiye ongolonjeza koma sakwanitsa, itana mulungu wako thawi zonse poti akalonjeza ndiyekhayo amakwanitsa ukadziwa izi sudzalilira chifukwa chamuthu nzako (AMEN)
Ngakhale wina atakuyesa kuti sindiwe ofunika kwa iyeyo, koma ngati iwe ndimulungu wako Pali ubale okwanila dziwa kuti zilibwino
Mulungu amadziwa chomwe iwe ukufuna ndipo sangalole kuti phazi lako leteleleke,tangokhulupilila kuti zomwe wapepha mulungu wamva🙏
Happy Sunday
Ngati kuli moyo omwe ukuvuta ndi kukhazikika moyo wauzimu, chifukwa ndichomwe chimaoneka chovuta ku chasamala,,,,koma ndifuna ndikulimbikitse kuti ngati kuli chithu chomwe chifunika kusamala ndi moyo wauzimu ngati mwa iwe mulibe chauzimu funafuna yesu kuti agonele mwa iwe ndikulamula moyo wako.
Pomwe tili mukhomaliro tiyeni timuyamike ambuye potifikitsa muthawi ino,tidziwa ena anadzuka ndimoyo koma pano muthawiso yomweyi achita ngozi,agonekedwa kuchipatala, pomwe Inu ndiine tili ndimoyo tangonena amen ngati muthawi imeneyi uli ndimoyo
Pomwe wadzuka ndimoyo lero tangonena ambuye zikomo chifukwa chamoyo mwandipatsaso lero nditsogoleleni patsikuli amen
Dear heavenly father lrejoice today at your word that's building my faith strong and influencing my actions . your word is my life, and the light that shows me how to walk on the path of victory prosperity, and success from day today in Jesus name amen.
PEMPHERO
Atate ndikufunani tsopano mukalamulile moyo wanga,mukakhale nane pamavuto komaso pamtendele,ndikafuna kukhala wachimwemwe thawi zonse za moyo wanga,mukandilimbikitse ndikuphuzila komaso ndikukhulupilila mawu anu,kachulukitseni masiku achimwemwe pamoyo wanga"ndiyamika inu poti simudzandisiya ndekha pitilizani kugonjetsa ondizinga , pitilizani kundipatsa zosowa zanga, mudzina lambuye wanthu yesu kristu Amen
Iwe amene ukuwelenga mulungu akwanilitse chosowa cha pamoyo wako
Chipambano chili kuseli kwa khondo limbikani pomenya khondo yomwe mulinayo kuti mupambane.
Matenda omwe ali pamwana wako ndikunenela mudzina lambuye wanthu yesu kristu kuti wachira Alleluyah
Chibwana chomwe ukuchita siya chifukwa mulungu akuona usayese kuti wapambana pomwe ulipo panja mulungu adziwa zamun'tima
Mau amene akuchoka pa mateyo 4vs18 ,,,,akutitsimikizila kuti pane Ife titsata yesu tidzakhala asodzi awanthu ,,, chifukwa yesu atakumana ndi Petro komaso Andrea yesu anati kwa iwo nditsateni,,,, ndikufuna kunena chiyani pa Inu okondedwa yesu akati timutsate tiyeni okondedwa mwambuye timutsate taonani kuti tikasiya ntchito zanthu zonyasa zomwe timachita ndikumtsata iye mulungu adzaika chokoma mwa Ife tiyeni tidziwitse azathu zabwino zomwe mulungu wachita kuti nawoso atsate yesu ,,,,, yambani Inu lero kuitanila azanu kwa yesu,,,, ambuye akudalitseni pokhala inu asodzi awanthu
Mwadzuka bwanji okondedwa mwambuye konse komwe muli?
Ulendo wina ulionse umayamba ndikuponya phazi limodzi kape giya imodzi ukaona kuti ukutheka ndipomwe umaonjeza phazi lina kapena giya ina apatu timati ulendo wathu ulibwino,,,koma nanga pomwe tikuyenda tikudziwa komwe ulendo wathu ukathele? dziwani kuti ulendo opanda cholinga umakhala ngati muthu amene mutu wake sumagwila ,,,lero dzifuseni kuti Kodi tsiku lanu laulendo mukadzanyamuka mudzafikila kuti GAHENA/PALADAISO? tiyeni tipange chisakho chokhala ndimalo ofikilako pathawi ya ulendo wathu ambuye akudalitseni.
Pomwe ena akuyesa ntchito yako kwa iwo silibwino, ndipomwe iwe ulimbike kugwila kuti adziwe kuti mulungu sachititsa manyazi olimbika, chaka chino utola chikwama chako chamadalitso tangolimbika kufulila kwa mulungu.
Morning
Ndikudziwa kuti watopa ndikupemphera mwina chomwe wakhala ukupepha koma mwina sukuyakhidwa ndifuna ndikulimbitse m'tima kuti mulungu akapeleka chako sichidzasowa chidzakhala chodekha komaso choopa mulungu,, chomwe mulinachocho musachinyoze mulungu alinacho cholinga chako sichimasowa chako sichiopsa chako chimakonda. Amen
God loves everyone poor and rich
Usadandaule pomwe nyengo zako sizikuyenda bwino dziwa kuti mulungu ndipomwe amafuna aone kukhulupilika kwako ,,,, yemwe akuyesa iwe opanda ntchito ndipomwe mulungu adzakutola ndipupuputa matope onse ndikupanga kukhala chida chake chodalilika ndipomwe mamuna unja ukufunayi adzapezeke,or nkazi unja ukufunayi mulungu adzakupatsa khala odikila.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Telephone
Website
Address
Blantyre
0981144698
Opening Hours
07:30 - 02:00 |
Machinjili, Khama
Blantyre, MACHINJILI,KHAMA
we sell good quality baby diapers and wipes at an affordable price
We Are In Blantyre Limbe Mahawa Arcade Opposite Nbs Bank Shop Number 26b Ground
Blantyre, BOX1212BT
Ginnery Mall
Blantyre
Welcome to our charming baby boutique, a haven for all things adorable and essential for your kids.
Victoria Avenue & Independence, Https://maps. App. Goo. Gl/icGSBrCoDrzYunEc 7
Blantyre, 265
All things baby, mommy and Maternity
Mall Of Africa, First Floor, Shop# B9, Ginnery Corner, Mw
Blantyre
stockist of quality children wear,essentials,furniture,decor, travel systems,toys and gifts.