Tadala
Tadala is a Malawian Hip Hop artist.
Munaawona Atcheya amatutumuka?
Lero chishango changa ndi yesu
Chotsa dzanja pa tsaya mchimwene!
Life is too short for so much sorrow.
Play the music, masula mtolo.
jNathan shot it
Pepa neighbor ngati zimakunyasha ๐จ
Mukachisi mwalowesa hustle
Yesu chachikhumi abusa ka mphatso
Pomwe ayimangilira
Anzawo tikulira
Si chamba nkafila maso
Maonekedwe anga mumaziwa ku judger
One thing I know zonse amaziwa ndi Jah Jah
Mumudziwe obadwila mu yudeya
Njala sizamva azandiuza uyu deya
Chipulumutso chikanakhala pa nsika
Ma prophet ambiri ali ndi mavenda
Munthu ndi munthu samayamika
Yopanda khini nsanje ndi matenda
Ndale ku guwa kuguwa nyanga
Bola ndimudziwe mlengi mu mtima mwanga
Ntchito za Mulungu palibe sungandipose
Nkuseseleka ndi malamulo ngati Mose
Pamene lipenga lidzalilanso
Mpamene ine sindidzalilanso
Pamene tidzamuona ndi maso
Tidzachoka mu m'dimaso
Nde chibaluwa ndizilembela mnyamata?
Apapa nde mwanama a Papa
Diamonds are forever.
Rest In Peace Jafali.
Akamwile to the world.
Tadala ndi ine. Koma Tadala ndi ife.
Skuva Fashions
Control those who control those who decide how long to cover a story and where it goes in the paper, and you control the news. Its politics everywhere.
Amayo koto,chaku mpoto wina amuphika ngati ali mu mpoto...
Stand Under The Music To Understand The Music
๐ฆโฏ๏ธ
Thanks to all the guys who participated this morning. Most of y'all got it right but unfortunately there could only be one winner.
BUT!
Heres another one. Four winners. 5k per winner.
Share the links,tag me and Sagonjah when you do. The most engaged posts will be our winners.
Remember, this one we'll get 4 winners for 5k per winner.
Links in the comment section
๐ฆโฏ๏ธ
The first person to correctly name the song title which has the lines below wins a TNM weekly bundle.
Lets go!!
"Chipulumutso chikanakhala pa msika
Ma prophet ambiri ali ma vendor
Munthu ndi munthu samayamika
Yopanda khini nsanje ndi matenda"
Good morning fam.
@7:30 we do another QuickQuiz.
TNM family, get ready.
Quick Quiz to airtel users and the first person to get it right will win a Mofaya weekly bundle.
Mention the song in Mtolo Vol. 2 which has the lines below
"Nde usaiwalire, usanandiwalire
Allah wa Ta'ala ndi ekha ndingamuswalire"
TNM users we go again madzulo.
๐คโฅ๏ธ๐
Sizokakamiza....
Chilungamo chimamasula...
Ndamvapo kuwawa ndayenela ku Stupa!
[MTOLO VOL. 2 LINKS IN THE COMMENT]
Guys, lero tikambilanepo pano!
To everyone who's listened to Mtolo Vol. 2, I'd love to know, whats your favorite jam so far?
Pepa neighbor ngati zimakunyasha!
Sagonjah x Tadala - Mtolo Vol. 2 Stream Mtolo Vol. 2, an album by Sagonjah x Tadala. Release Date: November 17, 2023.
Kuyamika mu zonse ngakhale zonse ndi chabe
๐คฒ
Osamatha mawu pama campaign
Tili Tonse bwanji ukundisungila ka mpeni
Ndikalowa m'boma zanga ndipakule
Chikwama cha mloma or mphasa ndiyalule
Ntchito kumalembana akubanja
Muzilimbikila kumatiuza akunjanja
Sitingaiwale wa nzeru asunga mawu
Samakhazikika okudya thako lagalu
Tadya nawo usipa matemba dzana lija
Likulemba lokha pa khoma dzanja lija
Ngati sakuwona muphamike mate mmaso
S***m ndi Gomorrah owelenga khala maso
Tawonana mawanga,mwangokoma pakamwa
Zonse sungaphangile tawonani mwatsamwa
Nde pano tadziwana
Chinamfuna m'bale chilipo
M'bale ife tidakalipo
Ndikupanga zanga
Mukubwela zanga ndikuphanga
Oyenda ndi mpeni ndi lako lidzakupha lupanga
Zimene nyuzipepala yalemba...
Saimba Ng'oma...
Ntcheu Classic tomorrow!
DON TARZ
Chizmo Njuchi
Blasto (IMVA!)
Saint-Realest
Queen Fyah
Backed by The Tuff Lionz International Band. Tikumane kumeneku mawa
Yo check it
Moyo umakoma ndi inu pambali
Mumandiuza zonse ndi nthawi sunga sabali
Keep your ears on the ground maso penya patali
Mukayankhula I have to listen, makani kwangali
Ndine dolo ndimadziwa
Moyo ndi madziwa
Samala masewela samachitila pa diwa
Khala olimbikila muli m'nyozo mu usiwa
Chisoni mkumatenda kuli zinkhani kusiwa
Dziwa adzakuiwala palibe chamuyaya
Dziwa ndi ife tadala kuli konse ukukhala
Khala chitsanzo, nthanga mu chipatso
Osaiwala kumapemphela moyo ndi mphatso
Palibe chingakulake
Ndiwe chimfana cha lucky
Nzeru za mwana zagona pakulemekeza make
Ndi atate
Siya phazi
Osakheza mwazi
Maso m'maso mwa munthu osayang'ana pansi
Pepa neighbor ngati zimakunyasha ๐จ๐ฅ๐
Satsogoza mthenga mavuto akamadza
Mu mtima kusandusa balaza
Mu bongo angozaza
Yekha yekha angodwedeza mutu wangofasa
Yekha yekha angolakhula zi nkhawa kusanza
Limenelo ndiye dziko mwakula
Limagiligisha limamanga nyakula
Kaya umapemphela umapanga maula
Pena zitenthe ngati uli kunsi kwa mbaula...
Hello ๐
Akuti sanamvelebe Mtolo Vol. 2?
Chifukwa chani? Muuzeni asadande.
Links in the comment section!
jNathan shot it
Kuyamika mu zonse ngakhale zonse ndi chabe
Zisachite kufika poti mpakana tikabe
Zochepazi ziphukile
Mtima wanga ukhutile
Ngati Chinga Gire nkabwelela mundichingamile
Zinsinsi za moyo mundiululire
Zipatso za moyo mundipululire
Moto wanyanya nkhuni mutifumulile
Dziko kuzungulira osadabwa zizungulire
Sinkumila ndikuyandama
Osaodzela ndikuyang'ana
Zisomo zake zingotsagana
Ndinali yani dzana
Lero ndine nyali dzana timangonamizana
Sinditama munthu kuwopa mwina andimana
Mu m'bwaa zanga ukhwepa
Panga zaine mpakana mtembo useka
Kumbwambwana ambwana
Kumazinyenga kupambana
Zako nzake, zake namana kumkhwapa napana
Now Playing: Amayi ft QUEST MW
Album: Mtolo 2
๐ฆโฏ๏ธ
Mtolo, Vol. 2 by Sagonjah & Tadala Album ยท 2023 ยท 9 Songs
Click here to claim your Sponsored Listing.